1Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira ndi zoyipa, iwe munthu wamphamvu?
2Tsiku lonse umakhalira kuganizira za kuwononga ena;
3Iwe umakonda choyipa mʼmalo mwa kuyankhula choonadi.
4Umakonda mawu onse opweteka,
5Zoonadi Mulungu adzakutsitsa kupita ku chiwonongeko chamuyaya:
6Olungama adzaona zimenezi ndi kuchita mantha;
7“Pano tsopano pali munthu
8Koma ine ndili ngati mtengo wa olivi
9Ine ndidzakutamandani kwamuyaya chifukwa cha zimene mwachita;