We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 52

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 51 Masalimo Masalimo 53 →

1Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira ndi zoyipa, iwe munthu wamphamvu?

2Tsiku lonse umakhalira kuganizira za kuwononga ena;

3Iwe umakonda choyipa mʼmalo mwa kuyankhula choonadi.

4Umakonda mawu onse opweteka,

5Zoonadi Mulungu adzakutsitsa kupita ku chiwonongeko chamuyaya:

6Olungama adzaona zimenezi ndi kuchita mantha;

7“Pano tsopano pali munthu

8Koma ine ndili ngati mtengo wa olivi

9Ine ndidzakutamandani kwamuyaya chifukwa cha zimene mwachita;

← Masalimo 51 Masalimo Masalimo 53 →