1Mundichitire chifundo, Inu Mulungu,
2Munditsuke zolakwa zanga zonse
3Pakuti ndikudziwa mphulupulu zanga,
4Motsutsana ndi Inu, Inu nokha, ndachimwa
5Zoonadi ine ndinali wochimwa pomwe ndimabadwa,
6Zoonadi inu mumafuna choonadi mu ziwalo zamʼkati mwanga;
7Mundiyeretse ndi hisope ndipo ndidzayera,
8Mundilole ndimve chimwemwe ndi chisangalalo,
9Mufulatire machimo anga
10Mulenge mʼkati mwanga mtima woyera Inu Mulungu
11Musandichotse pamaso panu
12Bwezeretsani mwa ine chimwemwe cha chipulumutso chanu
13Pamenepo ndidzaphunzitsa anthu amphulupulu njira zanu
14Mundipulumutse ku tchimo lokhetsa magazi, Inu Mulungu,
15Inu Ambuye tsekulani milomo yanga,
16Inu simusangalatsidwa ndi nsembe wamba.
17Nsembe za Mulungu ndi mzimu wosweka;
18Mwa kukoma mtima kwanu mupange Ziyoni kuti alemere;
19Kotero kudzakhala nsembe zachilungamo,