We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 51

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 50 Masalimo Masalimo 52 →

1Mundichitire chifundo, Inu Mulungu,

2Munditsuke zolakwa zanga zonse

3Pakuti ndikudziwa mphulupulu zanga,

4Motsutsana ndi Inu, Inu nokha, ndachimwa

5Zoonadi ine ndinali wochimwa pomwe ndimabadwa,

6Zoonadi inu mumafuna choonadi mu ziwalo zamʼkati mwanga;

7Mundiyeretse ndi hisope ndipo ndidzayera,

8Mundilole ndimve chimwemwe ndi chisangalalo,

9Mufulatire machimo anga

10Mulenge mʼkati mwanga mtima woyera Inu Mulungu

11Musandichotse pamaso panu

12Bwezeretsani mwa ine chimwemwe cha chipulumutso chanu

13Pamenepo ndidzaphunzitsa anthu amphulupulu njira zanu

14Mundipulumutse ku tchimo lokhetsa magazi, Inu Mulungu,

15Inu Ambuye tsekulani milomo yanga,

16Inu simusangalatsidwa ndi nsembe wamba.

17Nsembe za Mulungu ndi mzimu wosweka;

18Mwa kukoma mtima kwanu mupange Ziyoni kuti alemere;

19Kotero kudzakhala nsembe zachilungamo,

← Masalimo 50 Masalimo Masalimo 52 →