1Wamphamvuyo, Yehova Mulungu,
2Kuchokera ku Ziyoni, mokongola kwambiri
3Mulungu wathu akubwera ndipo sadzakhala chete;
4Iye akuyitanitsa zamumlengalenga
5Mundisonkhanitsire okhulupirika anga,
6Ndipo mayiko akumwamba akulengeza chilungamo chake,
7Imvani inu anthu anga, ndipo Ine ndidzayankhula,
8Sindikudzudzula chifukwa cha nsembe zako,
9Ine sindikufuna ngʼombe yayimuna kuchokera mʼkhola lako
10pakuti nyama iliyonse yakunkhalango ndi yanga
11Ine ndimadziwa mbalame iliyonse mʼmapiri
12Ndikanakhala ndi njala sindikanakuwuzani,
13Kodi ndimadya nyama ya ngʼombe zazimuna
14“Pereka nsembe zachiyamiko kwa Mulungu,
15Ndipo undiyitane pa tsiku lako la masautso;
16Koma kwa woyipa, Mulungu akuti,
17Iwe umadana ndi malangizo anga
18Ukaona wakuba umamutsatira,
19Umagwiritsa ntchito pakamwa pako pa zinthu zoyipa
20Nthawi zonse umayankhula motsutsana ndi mʼbale wako
21Wachita zimenezi ndipo Ine ndinali chete;
22“Ganizira izi, iwe amene umayiwala Mulungu
23Iye amene amapereka nsembe yamayamiko amandilemekeza,