We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 50

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 49 Masalimo Masalimo 51 →

1Wamphamvuyo, Yehova Mulungu,

2Kuchokera ku Ziyoni, mokongola kwambiri

3Mulungu wathu akubwera ndipo sadzakhala chete;

4Iye akuyitanitsa zamumlengalenga

5Mundisonkhanitsire okhulupirika anga,

6Ndipo mayiko akumwamba akulengeza chilungamo chake,

7Imvani inu anthu anga, ndipo Ine ndidzayankhula,

8Sindikudzudzula chifukwa cha nsembe zako,

9Ine sindikufuna ngʼombe yayimuna kuchokera mʼkhola lako

10pakuti nyama iliyonse yakunkhalango ndi yanga

11Ine ndimadziwa mbalame iliyonse mʼmapiri

12Ndikanakhala ndi njala sindikanakuwuzani,

13Kodi ndimadya nyama ya ngʼombe zazimuna

14“Pereka nsembe zachiyamiko kwa Mulungu,

15Ndipo undiyitane pa tsiku lako la masautso;

16Koma kwa woyipa, Mulungu akuti,

17Iwe umadana ndi malangizo anga

18Ukaona wakuba umamutsatira,

19Umagwiritsa ntchito pakamwa pako pa zinthu zoyipa

20Nthawi zonse umayankhula motsutsana ndi mʼbale wako

21Wachita zimenezi ndipo Ine ndinali chete;

22“Ganizira izi, iwe amene umayiwala Mulungu

23Iye amene amapereka nsembe yamayamiko amandilemekeza,

← Masalimo 49 Masalimo Masalimo 51 →