We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 49

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 48 Masalimo Masalimo 50 →

1Imvani izi anthu a mitundu yonse;

2anthu wamba pamodzi ndi anthu odziwika,

3Pakamwa panga padzayankhula mawu anzeru;

4Ndidzatchera khutu langa ku mwambo,

5Ine ndichitirenji mantha pamene masiku oyipa afika,

6Iwo amene adalira kulemera kwawo

7Palibe munthu amene angawombole moyo wa mnzake

8Dipo la moyo ndi la mtengowapatali,

9kuti iye akhale ndi moyo mpaka muyaya

10Pakuti onse amaona kuti anthu anzeru amamwalira;

11Manda awo adzakhala nyumba zawo mpaka muyaya,

12Ngakhale munthu akhale wachuma chotani,

13Izi ndi zimene zimachitikira iwo amene amadzidalira okha,

14Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda,

15Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda;

16Usavutike mu mtima pamene munthu akulemera,

17Pakuti sadzatenga kanthu pamodzi naye pamene wamwalira,

18Ngakhale pamene munthuyo ali moyo amadziyesa wodala,

19iyeyo adzakakhala pamodzi ndi mʼbado wa makolo ake,

20Munthu amene ali ndi chuma koma wopanda nzeru

← Masalimo 48 Masalimo Masalimo 50 →