1Wamkulu ndi Yehova, ndi woyenera kwambiri matamando
2Lokongola mu utali mwake,
3Mulungu ali mu malinga ake;
4Pamene mafumu anasonkhana pamodzi,
5iwo anaona mzindawo ndipo anadabwa kwambiri;
6Pomwepo anagwidwa nako kunjenjemera,
7Inu munawawononga monga sitima zapamadzi za ku Tarisisi
8Monga momwe tinamvera,
9Mʼkati mwa Nyumba yanu Mulungu,
10Monga dzina lanu, Inu Mulungu,
11Phiri la Ziyoni likukondwera,
12Yendayendani mu Ziyoni, uzungulireni mzindawo,
13Yangʼanitsitsani bwino mipanda yake,
14Pakuti Mulungu uyu ndi Mulungu wathu ku nthawi zosatha;