We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 47

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 46 Masalimo Masalimo 48 →

1Ombani mʼmanja, inu anthu onse;

2Ndi woopsadi Yehova Wammwambamwamba;

3Iye anatigonjetsera mitundu yambirimbiri ya anthu;

4Iye anatisankhira cholowa chathu,

5Mulungu wakwera, anthu akumufuwulira mwachimwemwe,

6Imbani matamando kwa Mulungu, imbani matamando;

7Pakuti Mulungu ndi mfumu ya dziko lonse lapansi;

8Mulungu akulamulira mitundu ya anthu;

9Anthu otchuka mwa anthu a mitundu ina asonkhana

← Masalimo 46 Masalimo Masalimo 48 →