1Ombani mʼmanja, inu anthu onse;
2Ndi woopsadi Yehova Wammwambamwamba;
3Iye anatigonjetsera mitundu yambirimbiri ya anthu;
4Iye anatisankhira cholowa chathu,
5Mulungu wakwera, anthu akumufuwulira mwachimwemwe,
6Imbani matamando kwa Mulungu, imbani matamando;
7Pakuti Mulungu ndi mfumu ya dziko lonse lapansi;
8Mulungu akulamulira mitundu ya anthu;
9Anthu otchuka mwa anthu a mitundu ina asonkhana