1Mulungu ndiye kothawira kwathu ndi mphamvu yathu,
2Nʼchifukwa chake sitidzaopa ngakhale dziko lapansi lisunthike,
3ngakhale madzi ake atakokoma ndi kuchita thovu,
4Kuli mtsinje umene njira zake za madzi zimasangalatsa mzinda wa Mulungu,
5Mulungu ali mʼkati mwake, iwo sudzagwa;
6Mitundu ikupokosera, mafumu akugwa;
7Yehova Wamphamvuzonse ali ndi ife,
8Bwerani kuti mudzaone ntchito za Yehova,
9Iye amathetsa nkhondo ku malekezero a dziko lapansi;
10Iye akuti, “Khala chete, ndipo dziwa kuti ndine Mulungu;
11Yehova Wamphamvuzonse ali ndi ife,