We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 45

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 44 Masalimo Masalimo 46 →

1Mtima wanga watakasika ndi nkhani yokoma

2Inu ndinu abwino kwambiri kuposa anthu onse

3Mangirirani lupanga lanu mʼchiwuno mwanu, inu munthu wamphamvu;

4Mu ukulu wanu mupite mutakwera mwachigonjetso

5Mivi yanu yakuthwa ilase mitima ya adani a mfumu,

6Mpando wanu waufumu, Inu Mulungu, udzakhala ku nthawi za nthawi;

7Inu mumakonda chilungamo ndi kudana ndi zoyipa;

8Mikanjo yanu yonse ndi yonunkhira ndi mure ndi aloe ndi kasiya;

9Ana aakazi a mafumu ali pakati pa akazi anu olemekezeka;

10Tamvera, iwe mwana wa mkazi ganizira ndipo tchera khutu;

11Mfumu yathedwa nzeru chifukwa cha kukongola kwako;

12Mwana wa mkazi wa ku Turo adzabwera ndi mphatso,

13Wokongola kwambiri ndi mwana wa mfumu ali mʼchipinda mwake,

14Atavala zovala zamaluwamaluwa akupita naye kwa mfumu;

15Iwo akuwaperekeza ndi chimwemwe ndi chisangalalo;

16Ana ako aamuna adzatenga malo a makolo ako;

17Ndidzabukitsa mbiri yako mʼmibado yonse;

← Masalimo 44 Masalimo Masalimo 46 →