1Chitsiru chimati mu mtima mwake,
2Mulungu kumwamba amayangʼana pansi pano
3Aliyense wabwerera,
4Kodi anthu ochita zoyipawa adzaphunziradi;
5Iwo anali pamenepo atathedwa nzeru ndi mantha aakulu
6Ndithu, chipulumutso cha Israeli nʼchochokera ku Ziyoni!