We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 41

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 40 Masalimo Masalimo 42 →

1Wodala ndi munthu amene amaganizira anthu osauka;

2Yehova adzamuteteza ndi kusunga moyo wake;

3Yehova adzamuthandiza pamene akudwala

4Ndinati, “Inu Yehova, mundichitire chifundo;

5Adani anga mwankhwidzi amanena za ine kuti,

6Pamene wina abwera kudzandiona,

7Adani anga onse amanongʼonezana pamodzi kulimbana nane,

8“Matenda owopsa amugwira;

9Ngakhale bwenzi langa la pamtima amene ndinamudalira,

10Koma Yehova mundichititre chifundo,

11Ine ndikudziwa kuti mukukondwera nane,

12Mu ungwiro wanga Inu mumandisunga

13Atamandike Yehova Mulungu wa Israeli

← Masalimo 40 Masalimo Masalimo 42 →