1Wodala ndi munthu amene amaganizira anthu osauka;
2Yehova adzamuteteza ndi kusunga moyo wake;
3Yehova adzamuthandiza pamene akudwala
4Ndinati, “Inu Yehova, mundichitire chifundo;
5Adani anga mwankhwidzi amanena za ine kuti,
6Pamene wina abwera kudzandiona,
7Adani anga onse amanongʼonezana pamodzi kulimbana nane,
8“Matenda owopsa amugwira;
9Ngakhale bwenzi langa la pamtima amene ndinamudalira,
10Koma Yehova mundichititre chifundo,
11Ine ndikudziwa kuti mukukondwera nane,
12Mu ungwiro wanga Inu mumandisunga
13Atamandike Yehova Mulungu wa Israeli