1Mofatsa ndinadikira Yehova
2Ananditulutsa mʼdzenje lachitayiko,
3Iye anayika nyimbo yatsopano mʼkamwa mwanga,
4Ndi wodala munthu
5Zambiri, Yehova Mulungu wanga,
6Nsembe ndi zopereka Inu simuzifuna,
7Kotero ndinati, “Ndili pano, ndabwera.
8Ndikufuna kuchita chifuniro chanu, Inu Mulungu wanga;
9Ndikulalikira uthenga wa chilungamo chanu mu msonkhano waukulu;
10Sindibisa chilungamo chanu mu mtima mwanga;
11Musandichotsere chifundo chanu Yehova;
12Pakuti mavuto osawerengeka andizungulira;
13Pulumutseni Yehova;
14Onse amene akufunafuna kuchotsa moyo wanga
15Iwo amene amanena kwa ine kuti, “Hee! Hee!”
16Koma iwo amene amafunafuna Inu
17Komabe Ine ndine wosauka ndi wosowa;