We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 39

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 38 Masalimo Masalimo 40 →

1Ndinati, “Ndidzasamalira njira zanga

2Koma pamene ndinali chete

3Mtima wanga unatentha mʼkati mwanga,

4“Yehova ndionetseni mathero a moyo wanga

5Inu mwachititsa kuti masiku anga akhale ochepa kwambiri,

6Munthu ali ngati chithunzithunzi chake pamene akuyenda uku ndi uku:

7“Koma tsopano Ambuye kodi ndifunanso chiyani?

8Pulumutseni ku zolakwa zanga zonse;

9Ine ndinali chete; sindinatsekule pakamwa panga

10Chotsani mkwapulo wanu pa ine;

11Inu mumadzudzula ndi kulanga anthu chifukwa cha tchimo lawo;

12“Imvani pemphero langa Inu Yehova,

13Musandiyangʼane mwaukali, choncho ndidzatha kusangalala

← Masalimo 38 Masalimo Masalimo 40 →