1Ndinati, “Ndidzasamalira njira zanga
2Koma pamene ndinali chete
3Mtima wanga unatentha mʼkati mwanga,
4“Yehova ndionetseni mathero a moyo wanga
5Inu mwachititsa kuti masiku anga akhale ochepa kwambiri,
6Munthu ali ngati chithunzithunzi chake pamene akuyenda uku ndi uku:
7“Koma tsopano Ambuye kodi ndifunanso chiyani?
8Pulumutseni ku zolakwa zanga zonse;
9Ine ndinali chete; sindinatsekule pakamwa panga
10Chotsani mkwapulo wanu pa ine;
11Inu mumadzudzula ndi kulanga anthu chifukwa cha tchimo lawo;
12“Imvani pemphero langa Inu Yehova,
13Musandiyangʼane mwaukali, choncho ndidzatha kusangalala