We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 38

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 37 Masalimo Masalimo 39 →

1Yehova musandidzudzule mutapsa mtima

2Pakuti mivi yanu yandilasa,

3Chifukwa cha ukali wanu mulibe thanzi mʼthupi langa;

4Kulakwa kwanga kwandipsinja

5Mabala anga akuwola ndipo akununkha

6Ine ndapindika msana ndipo ndawerama kwambiri;

7Msana wanga wagwidwa ndi ululu wosasimbika,

8Ndilibe mphamvu ndipo ndakunthidwa kwathunthu;

9Zokhumba zanga zonse zili poonekera pamaso panu Ambuye,

10Mtima wanga ukugunda, mphamvu zanga zikutha;

11Abwenzi anga ndi anzanga akundipewa chifukwa cha mabala anga;

12Iwo amene akufunafuna moyo wanga atchera misampha yawo,

13Ine ndili ngati munthu wosamva amene sangamve,

14Ndakhala ngati munthu amene samva,

15Ndikudikira Inu Yehova;

16Pakuti Ine ndinati, “Musawalole kuti akondwere

17Pakuti ndili pafupi kugwa,

18Ndikuvomereza mphulupulu zanga;

19Ambiri ndi adani anga amphamvu;

20Iwo amene amandibwezera zoyipa mʼmalo mwa zabwino

21Inu Yehova, musanditaye;

22Bwerani msanga kudzandithandiza,

← Masalimo 37 Masalimo Masalimo 39 →