1Yehova musandidzudzule mutapsa mtima
2Pakuti mivi yanu yandilasa,
3Chifukwa cha ukali wanu mulibe thanzi mʼthupi langa;
4Kulakwa kwanga kwandipsinja
5Mabala anga akuwola ndipo akununkha
6Ine ndapindika msana ndipo ndawerama kwambiri;
7Msana wanga wagwidwa ndi ululu wosasimbika,
8Ndilibe mphamvu ndipo ndakunthidwa kwathunthu;
9Zokhumba zanga zonse zili poonekera pamaso panu Ambuye,
10Mtima wanga ukugunda, mphamvu zanga zikutha;
11Abwenzi anga ndi anzanga akundipewa chifukwa cha mabala anga;
12Iwo amene akufunafuna moyo wanga atchera misampha yawo,
13Ine ndili ngati munthu wosamva amene sangamve,
14Ndakhala ngati munthu amene samva,
15Ndikudikira Inu Yehova;
16Pakuti Ine ndinati, “Musawalole kuti akondwere
17Pakuti ndili pafupi kugwa,
18Ndikuvomereza mphulupulu zanga;
19Ambiri ndi adani anga amphamvu;
20Iwo amene amandibwezera zoyipa mʼmalo mwa zabwino
21Inu Yehova, musanditaye;
22Bwerani msanga kudzandithandiza,