We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 37

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 36 Masalimo Masalimo 38 →

1Usamavutike chifukwa cha anthu oyipa

2pakuti monga udzu iwo adzafota msanga,

3Khulupirira Yehova ndipo uzichita zabwino;

4Udzikondweretse wekha mwa Yehova

5Pereka njira yako kwa Yehova;

6Iye adzachititsa chilungamo chako kuwala ngati mʼbandakucha,

7Khala chete pamaso pa Yehova ndipo umudikire mofatsa;

8Pewa kupsa mtima ndipo tembenuka kuchoka ku ukali,

9Pakuti anthu oyipa adzachotsedwa,

10Kwa kanthawi oyipa sadzapezekanso;

11Koma ofatsa adzalandira dziko

12Oyipa amakonza chiwembu kutsutsana ndi olungama

13koma Ambuye amaseka oyipa

14Oyipa amasolola lupanga

15Koma malupanga awo analasa mitima yawo yomwe,

16Zabwino zochepa zimene olungama ali nazo

17pakuti mphamvu ya oyipa idzasweka,

18Masiku a anthu osalakwa amadziwika ndi Yehova,

19Pa nthawi ya mavuto iwo sadzafota;

20Koma oyipa adzawonongeka;

21Oyipa amabwereka ndipo sabweza

22Iwo amene Yehova amawadalitsa adzalandira dziko,

23Ngati Yehova akondwera ndi njira ya munthu,

24ngakhale atapunthwa sadzagwa,

25Ine ndinali wamngʼono ndipo tsopano ndakalamba

26Iwo ndi owolowamanja nthawi zonse ndipo amabwereketsa mwaufulu;

27Tembenuka kuchoka ku zoyipa ndipo chita zabwino;

28Pakuti Yehova amakonda wolungama

29olungama adzalandira dziko

30Pakamwa pa munthu wolungama pamayankhula za nzeru,

31Lamulo la Mulungu wake lili mu mtima mwake;

32Oyipa amabisala kudikira olungama;

33koma Yehova sadzawasiya pansi pa mphamvu yawo

34Khulupirira Yehova,

35Ine ndinaona munthu woyipa ndi munthu wopanda chifundo

36Koma sanachedwe kumwalira ndipo sanaonekenso;

37Ganizira za munthu wosalakwa, yangʼanitsitsa munthu wolungama;

38Koma anthu ochimwa adzawonongeka;

39Chipulumutso cha olungama chimachokera kwa Yehova;

40Yehova amawathandiza ndi kuwalanditsa;

← Masalimo 36 Masalimo Masalimo 38 →