1Uthenga uli mu mtima mwanga
2Pakuti iye mʼkuona kwake amadzinyenga yekha kwambiri,
3Mawu a pakamwa pake ndi oyipa ndi achinyengo;
4Ngakhale ali pa bedi pake amakonzekera zoyipa;
5Chikondi chanu Yehova, chimafika ku mayiko a kumwamba,
6Chilungamo chanu Mulungu chili ngati mapiri aakulu,
7Chikondi chanu chosatha ndi chamtengowapatali!
8Iwo amadyerera zinthu zambiri za mʼnyumba yanu;
9Pakuti kwa Inu kuli kasupe wamoyo;
10Pitirizani chikondi chanu pa iwo amene amakudziwani,
11Musalole kuti phazi la wodzikuza libwere kulimbana nane,
12Onani momwe ochita zoyipa agonera atagwa,