We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 36

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 35 Masalimo Masalimo 37 →

1Uthenga uli mu mtima mwanga

2Pakuti iye mʼkuona kwake amadzinyenga yekha kwambiri,

3Mawu a pakamwa pake ndi oyipa ndi achinyengo;

4Ngakhale ali pa bedi pake amakonzekera zoyipa;

5Chikondi chanu Yehova, chimafika ku mayiko a kumwamba,

6Chilungamo chanu Mulungu chili ngati mapiri aakulu,

7Chikondi chanu chosatha ndi chamtengowapatali!

8Iwo amadyerera zinthu zambiri za mʼnyumba yanu;

9Pakuti kwa Inu kuli kasupe wamoyo;

10Pitirizani chikondi chanu pa iwo amene amakudziwani,

11Musalole kuti phazi la wodzikuza libwere kulimbana nane,

12Onani momwe ochita zoyipa agonera atagwa,

← Masalimo 35 Masalimo Masalimo 37 →