We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 35

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 34 Masalimo Masalimo 36 →

1Inu Yehova, mulimbane nawo amene akulimbana nane;

2Tengani chishango ndi lihawo;

3Tengani mkondo ndi nthungo,

4Iwo amene akufunafuna moyo wanga

5Akhale ngati mankhusu owuluka ndi mphepo

6Njira yawo ikhale ya mdima ndi yoterera

7Popeza ananditchera ukonde popanda chifukwa

8chiwonongeko chiwapeza modzidzimutsa

9Pamenepo moyo wanga udzakondwera mwa Yehova

10Thupi langa lidzafuwula mokondwera,

11Mboni zopanda chisoni zinayimirira,

12Iwo anandibwezera zoyipa pa zabwino

13Koma pamene iwo ankadwala, ine ndinavala chiguduli

14ndinayendayenda ndi kulira maliro,

15Koma pamene ndinaphunthwa, iwo anasonkhana mosangalala;

16Monga anthu osapembedza, iwo anandinyoza mwachipongwe;

17Ambuye, mpaka liti mudzakhala mukungoyangʼana?

18Ndidzakuyamikani mu msonkhano waukulu;

19Musalole adani anga onyenga

20Iwowo sayankhula mwamtendere,

21Iwo amandiseka mofuwula ndipo amati, “Haa! Haa!

22Yehova mwaona zimenezi; musakhale chete.

23Dzukani, ndipo nyamukani kunditeteza!

24Onetsani kusalakwa kwanga mwa chilungamo chanu, Inu Yehova Mulungu wanga.

25Musalole kuti aganize kuti, “Amati atani, zachitika monga momwe timafunira!”

26Onse amene amakondwera ndi masautso anga

27Koma amene amakondwera chifukwa chakuti ndine wosalakwa,

28Pakamwa panga padzayankhula za chilungamo chanu

← Masalimo 34 Masalimo Masalimo 36 →