We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 34

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 33 Masalimo Masalimo 35 →

1Ndidzayamika Yehova nthawi zonse;

2Moyo wanga udzanyadira Yehova;

3Lemekezani Yehova pamodzi ndi ine;

4Ine ndinafunafuna Yehova ndipo Iye anandiyankha;

5Iwo amene amayangʼana kwa Iye, nkhope zawo zimanyezimira;

6Munthu wosauka uno anayitana, ndipo Yehova anamumva;

7Mngelo wa Yehova amatchinjiriza amene amakonda Iye

8Lawani ndipo onani kuti Yehova ndi wabwino;

9Wopani Yehova inu oyera mtima ake,

10Mikango itha kulefuka ndi kumva njala

11Bwerani ana anga, mundimvere;

12Aliyense wa inu amene amakonda moyo wake

13asunge lilime lake ku zoyipa

14Tembenuka kuchoka ku zoyipa ndipo chita zabwino;

15Maso a Yehova ali pa olungama

16nkhope ya Yehova ikutsutsana ndi amene amachita zoyipa,

17Olungama amafuwula, ndipo Yehova amawamva;

18Yehova ali pafupi kwa osweka mtima

19Munthu wolungama atha kukhala ndi mavuto ambiri,

20Iye amateteza mafupa ake onse,

21Choyipa chidzapha anthu oyipa;

22Yehova amawombola atumiki ake;

← Masalimo 33 Masalimo Masalimo 35 →