1Ndidzayamika Yehova nthawi zonse;
2Moyo wanga udzanyadira Yehova;
3Lemekezani Yehova pamodzi ndi ine;
4Ine ndinafunafuna Yehova ndipo Iye anandiyankha;
5Iwo amene amayangʼana kwa Iye, nkhope zawo zimanyezimira;
6Munthu wosauka uno anayitana, ndipo Yehova anamumva;
7Mngelo wa Yehova amatchinjiriza amene amakonda Iye
8Lawani ndipo onani kuti Yehova ndi wabwino;
9Wopani Yehova inu oyera mtima ake,
10Mikango itha kulefuka ndi kumva njala
11Bwerani ana anga, mundimvere;
12Aliyense wa inu amene amakonda moyo wake
13asunge lilime lake ku zoyipa
14Tembenuka kuchoka ku zoyipa ndipo chita zabwino;
15Maso a Yehova ali pa olungama
16nkhope ya Yehova ikutsutsana ndi amene amachita zoyipa,
17Olungama amafuwula, ndipo Yehova amawamva;
18Yehova ali pafupi kwa osweka mtima
19Munthu wolungama atha kukhala ndi mavuto ambiri,
20Iye amateteza mafupa ake onse,
21Choyipa chidzapha anthu oyipa;
22Yehova amawombola atumiki ake;