We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 42

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 41 Masalimo Masalimo 43 →

1Monga mbawala ipuma wefuwefu kufunafuna mitsinje yamadzi,

2Moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Mulungu, lofuna Mulungu wamoyo.

3Misozi yanga yakhala chakudya changa

4Zinthu izi ndimazikumbukira

5Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni, iwe moyo wanga?

6Mulungu wanga.

7Madzi akuya akuyitana madzi akuya

8Koma usana Yehova amalamulira chikondi chake,

9Ine ndikuti kwa Mulungu Thanthwe langa,

10Mafupa anga ali ndi ululu wakufa nawo

11Bwanji ukumva chisoni,

← Masalimo 41 Masalimo Masalimo 43 →