1Monga mbawala ipuma wefuwefu kufunafuna mitsinje yamadzi,
2Moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Mulungu, lofuna Mulungu wamoyo.
3Misozi yanga yakhala chakudya changa
4Zinthu izi ndimazikumbukira
5Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni, iwe moyo wanga?
6Mulungu wanga.
7Madzi akuya akuyitana madzi akuya
8Koma usana Yehova amalamulira chikondi chake,
9Ine ndikuti kwa Mulungu Thanthwe langa,
10Mafupa anga ali ndi ululu wakufa nawo
11Bwanji ukumva chisoni,