1Ngodala munthu
2Ngodala munthu
3Pamene ndinali chete,
4Pakuti usana ndi usiku
5Kotero ine ndinavomereza tchimo langa kwa Inu,
6Choncho aliyense okhulupirika apemphere kwa Inuyo
7Inu ndi malo anga obisala;
8Ndidzakulangiza ndi kukuphunzitsa njira imene udzayendamo;
9Usakhale ngati kavalo kapena bulu,
10Zowawa ndi zambiri za anthu oyipa
11Kondwerani mwa Yehova inu olungama;