1Mwa Inu Yehova, ine ndimathawiramo;
2Tcherani khutu lanu kwa ine,
3Popeza Inu ndinu thanthwe langa ndi linga langa,
4Ndimasuleni mu msampha umene anditchera
5Mʼmanja mwanu ndipereka mzimu wanga;
6Koma ine ndimadana nawo amene amamamatira mafano achabechabe;
7Ndidzakondwa ndi kusangalala mʼchikondi chanu
8Inu simunandipereke kwa mdani
9Mundichitire chifundo Inu Yehova pakuti ndili pa mavuto;
10Moyo wanga ukunyeka chifukwa cha kuwawidwa mtima
11Chifukwa cha adani anga onse,
12Ine ndinayiwalika kwa iwo ngati kuti ndinamwalira;
13Pakuti ine ndamva zonena zoyipa za anthu ambiri;
14Koma ndikudalira Inu Yehova;
15Masiku anga ali mʼmanja mwanu;
16Walitsani nkhope yanu pa mtumiki wanu;
17Yehova musalole kuti ndichite manyazi,
18Milomo yawo yabodzayo ikhale chete,
19Ndi waukulu ubwino wanu
20Mu mthunzi wa pamalo popezeka panu muwabisa,
21Matamando akhale kwa Yehova,
22Ndili mʼnkhawa zanga ndinati,
23Kondani Yehova oyera mtima ake onse!
24Khalani ndi nyonga ndipo limbani mtima,