1Ndidzakukwezani Yehova,
2Inu Yehova Mulungu wanga ndinapempha kwa Inu thandizo
3Inu Yehova, munanditulutsa ku manda,
4Imbirani Yehova inu anthu ake okhulupirika;
5Pakuti mkwiyo wake umakhala kwa kanthawi
6Pamene ndinaona kuti ndili otetezedwa ndinati,
7Inu Yehova, pamene munandikomera mtima,
8Kwa Inu Yehova ndinayitana;
9“Kodi pali phindu lanji powonongeka kwanga
10Imvani Yehova ndipo mundichitire chifundo;
11Inu munasandutsa kulira kwanga kukhala kuvina;
12kuti mtima wanga uthe kuyimbira Inu usakhale chete.