We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 30

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 29 Masalimo Masalimo 31 →

1Ndidzakukwezani Yehova,

2Inu Yehova Mulungu wanga ndinapempha kwa Inu thandizo

3Inu Yehova, munanditulutsa ku manda,

4Imbirani Yehova inu anthu ake okhulupirika;

5Pakuti mkwiyo wake umakhala kwa kanthawi

6Pamene ndinaona kuti ndili otetezedwa ndinati,

7Inu Yehova, pamene munandikomera mtima,

8Kwa Inu Yehova ndinayitana;

9“Kodi pali phindu lanji powonongeka kwanga

10Imvani Yehova ndipo mundichitire chifundo;

11Inu munasandutsa kulira kwanga kukhala kuvina;

12kuti mtima wanga uthe kuyimbira Inu usakhale chete.

← Masalimo 29 Masalimo Masalimo 31 →