We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 29

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 28 Masalimo Masalimo 30 →

1Perekani kwa Yehova, inu anthu amphamvu,

2Perekani kwa Yehova ulemerero woyenera dzina lake,

3Liwu la Yehova lili pamwamba pa madzi;

4Liwu la Yehova ndi lamphamvu;

5Liwu la Yehova limathyola mikungudza;

6Iye amachititsa Lebanoni kulumphalumpha ngati mwana wangʼombe,

7Liwu la Yehova limakantha

8Liwu la Yehova limagwedeza chipululu;

9Liwu la Yehova limapindapinda mibawa

10Yehova amakhala pamwamba pa madzi osefukira,

11Yehova amapereka mphamvu kwa anthu ake;

← Masalimo 28 Masalimo Masalimo 30 →