1Perekani kwa Yehova, inu anthu amphamvu,
2Perekani kwa Yehova ulemerero woyenera dzina lake,
3Liwu la Yehova lili pamwamba pa madzi;
4Liwu la Yehova ndi lamphamvu;
5Liwu la Yehova limathyola mikungudza;
6Iye amachititsa Lebanoni kulumphalumpha ngati mwana wangʼombe,
7Liwu la Yehova limakantha
8Liwu la Yehova limagwedeza chipululu;
9Liwu la Yehova limapindapinda mibawa
10Yehova amakhala pamwamba pa madzi osefukira,
11Yehova amapereka mphamvu kwa anthu ake;