1Kwa Inu ine ndiyitana, Yehova ndinu Thanthwe langa;
2Imvani kupempha chifundo kwanga
3Musandikokere kutali pamodzi ndi anthu oyipa,
4Muwabwezere chifukwa cha zochita zawo
5Popeza iwowo sakhudzidwa ndi ntchito za Yehova,
6Matamando apite kwa Yehova,
7Yehova ndiye mphamvu yanga ndi chishango changa;
8Yehova ndi mphamvu ya anthu ake,
9Pulumutsani anthu anu ndipo mudalitse cholowa chanu;