We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 28

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 27 Masalimo Masalimo 29 →

1Kwa Inu ine ndiyitana, Yehova ndinu Thanthwe langa;

2Imvani kupempha chifundo kwanga

3Musandikokere kutali pamodzi ndi anthu oyipa,

4Muwabwezere chifukwa cha zochita zawo

5Popeza iwowo sakhudzidwa ndi ntchito za Yehova,

6Matamando apite kwa Yehova,

7Yehova ndiye mphamvu yanga ndi chishango changa;

8Yehova ndi mphamvu ya anthu ake,

9Pulumutsani anthu anu ndipo mudalitse cholowa chanu;

← Masalimo 27 Masalimo Masalimo 29 →