1Yehova ndiye kuwunika kwanga ndi chipulumutso changa;
2Pamene anthu oyipa abwera kudzalimbana nane
3Ngakhale gulu lankhondo lindizinge,
4Chinthu chimodzi chokha chimene ndipempha kwa Yehova,
5Pakuti pa tsiku la msautso
6Kotero mutu wanga udzakwezedwa
7Imvani mawu anga pamene ndiyitana Inu Yehova
8Mtima wanga ukuti kwa Inu, “Funafuna nkhope yake!”
9Musandibisire nkhope yanu,
10Ngakhale abambo ndi amayi anga anditaya
11Phunzitseni njira yanu Inu Yehova,
12Musandipereke ku zokhumba za adani anga,
13Ine ndikutsimikiza mtima za zimenezi;
14Dikirani pa Yehova;