We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 27

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 26 Masalimo Masalimo 28 →

1Yehova ndiye kuwunika kwanga ndi chipulumutso changa;

2Pamene anthu oyipa abwera kudzalimbana nane

3Ngakhale gulu lankhondo lindizinge,

4Chinthu chimodzi chokha chimene ndipempha kwa Yehova,

5Pakuti pa tsiku la msautso

6Kotero mutu wanga udzakwezedwa

7Imvani mawu anga pamene ndiyitana Inu Yehova

8Mtima wanga ukuti kwa Inu, “Funafuna nkhope yake!”

9Musandibisire nkhope yanu,

10Ngakhale abambo ndi amayi anga anditaya

11Phunzitseni njira yanu Inu Yehova,

12Musandipereke ku zokhumba za adani anga,

13Ine ndikutsimikiza mtima za zimenezi;

14Dikirani pa Yehova;

← Masalimo 26 Masalimo Masalimo 28 →