1Weruzeni Inu Yehova
2Patseni mayeso, Inu Yehova ndipo ndiyeseni,
3pakuti chikondi chanu chili pamaso panga nthawi zonse,
4Ine sindikhala pansi pamodzi ndi anthu achinyengo,
5Ndimanyansidwa ndi msonkhano wa anthu ochita zoyipa
6Ndimasamba mʼmanja mwanga kuonetsa kusalakwa kwanga
7kulengeza mofuwula za matamando anu
8Ndimakonda Nyumba imene Inu Yehova mumakhalamo,
9Musachotse moyo wanga pamodzi ndi ochimwa,
10amene mʼmanja mwawo muli ndondomeko zoyipa,
11Koma ine ndimakhala moyo wosalakwa;
12Ndayima pa malo wopanda zovuta