We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 26

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 25 Masalimo Masalimo 27 →

1Weruzeni Inu Yehova

2Patseni mayeso, Inu Yehova ndipo ndiyeseni,

3pakuti chikondi chanu chili pamaso panga nthawi zonse,

4Ine sindikhala pansi pamodzi ndi anthu achinyengo,

5Ndimanyansidwa ndi msonkhano wa anthu ochita zoyipa

6Ndimasamba mʼmanja mwanga kuonetsa kusalakwa kwanga

7kulengeza mofuwula za matamando anu

8Ndimakonda Nyumba imene Inu Yehova mumakhalamo,

9Musachotse moyo wanga pamodzi ndi ochimwa,

10amene mʼmanja mwawo muli ndondomeko zoyipa,

11Koma ine ndimakhala moyo wosalakwa;

12Ndayima pa malo wopanda zovuta

← Masalimo 25 Masalimo Masalimo 27 →