1Kwa Inu Yehova, ndipereka moyo wanga.
2Ndimadalira Inu Mulungu wanga.
3Aliyense amene amayembekezera kwa Ambuye
4Ndidziwitseni njira zanu Inu Yehova,
5tsogolereni mʼchoonadi chanu ndi kundiphunzitsa,
6Kumbukirani Inu Yehova chifundo ndi chikondi chanu chachikulu,
7Musakumbukire machimo a ubwana wanga
8Yehova ndi wabwino ndi wolungama;
9Amatsogolera odzichepetsa kuti achite zolungama
10Njira zonse za Yehova ndi zachikondi ndi zokhulupirika
11Chifukwa cha dzina lanu, Inu Yehova,
12Tsono ndani munthu amene amaopa Yehova?
13Iye adzakhala pa ulemerero masiku ake onse,
14Yehova amawulula chinsinsi chake kwa iwo amene amamuopa;
15Maso anga ali pa Yehova nthawi zonse,
16Tembenukirani kwa ine ndipo mundikomere mtima,
17Masautso a mu mtima mwanga achulukirachulukira;
18Penyani mazunzo anga ndi zovuta zanga
19Onani mmene adani anga achulukira
20Tetezani moyo wanga ndi kundilanditsa;
21Kukhulupirika ndi kulungama kwanga kunditeteze,
22Wombolani Israeli Inu Mulungu,