1Dziko lapansi ndi la Yehova ndi zonse zimene zili mʼmenemo,
2pakuti Iye ndiye anayika maziko ake pa nyanja
3Ndani angakwere phiri la Yehova?
4Iye amene ali ndi mʼmanja moyera ndi mtima woyera,
5Iyeyo adzalandira madalitso kwa Yehova
6Umenewo ndiwo mʼbado wa amene amafunafuna Yehova;
7Tukulani mitu yanu inu zipata;
8Kodi Mfumu yaulemereroyo ndani?
9Tukulani mitu yanu, inu zipata;
10Kodi Mfumu yaulemereroyo ndani?