We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 21

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 20 Masalimo Masalimo 22 →

1Inu Yehova, mfumu ikusangalala mu mphamvu yanu,

2Inu mwayipatsa zokhumba za mtima wake

3Inu munayilandira ndi madalitso ochuluka

4Iye anakupemphani moyo, ndipo munamupatsa

5Kudzera mʼzigonjetso zimene munapereka, ulemerero wake ndi waukulu;

6Zoonadi Inu mwayipatsa madalitso amuyaya,

7Pakuti mfumu imadalira Yehova;

8Dzanja lanu lidzayimitsa adani anu onse;

9Pa nthawi ya kuonekera kwanu

10Inu mudzawononga ana awo pa dziko lapansi,

11Ngakhale iwo akukonzereni chiwembu mwa kuchenjera kwawo

12pakuti mudzawapirikitsa ndipo adzaonetsa misana yawo

13Mukwezeke Inu Yehova mʼmphamvu yanu,

← Masalimo 20 Masalimo Masalimo 22 →