We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 22

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 21 Masalimo Masalimo 23 →

1Mulungu wanga, Mulungu wanga, nʼchifukwa chiyani mwandisiya?

2Inu Mulungu wanga, ine ndimalira masana, koma simuyankha,

3Inu ndinu Woyera, wokhala pa mpando waufumu;

4Pa inu makolo athu anadalira;

5Analirira kwa inu ndipo munawapulumutsa.

6Koma ine ndine nyongolotsi osati munthu,

7Onse amene amandiona amandiseka;

8“Iyeyu amadalira Yehova,

9Komabe Inu ndinu amene munandibadwitsa, munanditulutsa mʼmimba mwa amayi anga.

10Chibadwire ine ndinaperekedwa kwa Inu;

11Musakhale kutali ndi ine,

12Ngʼombe zazimuna zandizungulira;

13Mikango yobangula pokadzula nyama,

14Ine ndatayika pansi ngati madzi

15Mphamvu zanga zauma ngati phale,

16Agalu andizungulira;

17Ine nditha kuwerenga mafupa anga onse;

18Iwo agawana zovala zanga pakati pawo

19Koma Inu Yehova, musakhale kutali;

20Pulumutsani moyo wanga ku lupanga,

21Ndilanditseni mʼkamwa mwa mikango;

22Ine ndidzalengeza dzina lanu kwa abale anga;

23Inu amene mumaopa Yehova mutamandeni!

24Pakuti Iye sanapeputse kapena kunyoza

25Ndidzakutamandani pa msonkhano waukulu chifukwa cha zimene mwandichitira.

26Osauka adzadya ndipo adzakhuta;

27Malekezero onse a dziko lapansi

28pakuti ulamuliro ndi wake wa Yehova

29Anthu olemera onse a dziko lapansi adzachita phwando ndi kulambira;

30Zidzukulu zamʼtsogolo zidzamutumikira Iye;

31Iwo adzalengeza za chilungamo chake

← Masalimo 21 Masalimo Masalimo 23 →