1Mulungu wanga, Mulungu wanga, nʼchifukwa chiyani mwandisiya?
2Inu Mulungu wanga, ine ndimalira masana, koma simuyankha,
3Inu ndinu Woyera, wokhala pa mpando waufumu;
4Pa inu makolo athu anadalira;
5Analirira kwa inu ndipo munawapulumutsa.
6Koma ine ndine nyongolotsi osati munthu,
7Onse amene amandiona amandiseka;
8“Iyeyu amadalira Yehova,
9Komabe Inu ndinu amene munandibadwitsa, munanditulutsa mʼmimba mwa amayi anga.
10Chibadwire ine ndinaperekedwa kwa Inu;
11Musakhale kutali ndi ine,
12Ngʼombe zazimuna zandizungulira;
13Mikango yobangula pokadzula nyama,
14Ine ndatayika pansi ngati madzi
15Mphamvu zanga zauma ngati phale,
16Agalu andizungulira;
17Ine nditha kuwerenga mafupa anga onse;
18Iwo agawana zovala zanga pakati pawo
19Koma Inu Yehova, musakhale kutali;
20Pulumutsani moyo wanga ku lupanga,
21Ndilanditseni mʼkamwa mwa mikango;
22Ine ndidzalengeza dzina lanu kwa abale anga;
23Inu amene mumaopa Yehova mutamandeni!
24Pakuti Iye sanapeputse kapena kunyoza
25Ndidzakutamandani pa msonkhano waukulu chifukwa cha zimene mwandichitira.
26Osauka adzadya ndipo adzakhuta;
27Malekezero onse a dziko lapansi
28pakuti ulamuliro ndi wake wa Yehova
29Anthu olemera onse a dziko lapansi adzachita phwando ndi kulambira;
30Zidzukulu zamʼtsogolo zidzamutumikira Iye;
31Iwo adzalengeza za chilungamo chake