1Yehova akuyankhe pamene uli pa msautso;
2Iye atumize thandizo kuchokera ku malo ake opatulika;
3Iye akumbukire nsembe zako zonse
4Akupatse chokhumba cha mtima wako
5Ife tidzafuwula ndi chimwemwe pamene iwe wapambana
6Tsopano ndadziwa kuti Yehova amapulumutsa wodzozedwa wake;
7Ena amadalira magaleta ndipo ena akavalo
8Iwo amagonjetsedwa ndi kugwa,
9Inu Yehova, pulumutsani mfumu!