We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 20

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 19 Masalimo Masalimo 21 →

1Yehova akuyankhe pamene uli pa msautso;

2Iye atumize thandizo kuchokera ku malo ake opatulika;

3Iye akumbukire nsembe zako zonse

4Akupatse chokhumba cha mtima wako

5Ife tidzafuwula ndi chimwemwe pamene iwe wapambana

6Tsopano ndadziwa kuti Yehova amapulumutsa wodzozedwa wake;

7Ena amadalira magaleta ndipo ena akavalo

8Iwo amagonjetsedwa ndi kugwa,

9Inu Yehova, pulumutsani mfumu!

← Masalimo 19 Masalimo Masalimo 21 →