1Zakumwamba zimalengeza za ulemerero wa Mulungu;
2Tsiku ndi tsiku zimayankhula mawu ambiri,
3Palibe kuyankhula, palibe mawu aliwonse;
4Koma uthenga wawo umapita pa dziko lonse lapansi,
5Dzuwa lili ngati mkwatibwi wobwera kuchokera ku nsanja yake,
6Limatuluka kuyambira mbali ina ya thambo
7Lamulo la Yehova ndi langwiro,
8Malangizo a Yehova ndi olungama,
9Kuopa Yehova ndiye chinthu changwiro,
10ndi a mtengowapatali kuposa golide,
11Mtumiki wanu amachenjezedwa nawo;
12Ndani angathe kudziwa zolakwa zake?
13Muteteze mtumiki wanunso ku machimo ochita akudziwa;
14Mawu a mʼkamwa mwanga ndi zolingalira za mu mtima mwanga