We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 19

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 18 Masalimo Masalimo 20 →

1Zakumwamba zimalengeza za ulemerero wa Mulungu;

2Tsiku ndi tsiku zimayankhula mawu ambiri,

3Palibe kuyankhula, palibe mawu aliwonse;

4Koma uthenga wawo umapita pa dziko lonse lapansi,

5Dzuwa lili ngati mkwatibwi wobwera kuchokera ku nsanja yake,

6Limatuluka kuyambira mbali ina ya thambo

7Lamulo la Yehova ndi langwiro,

8Malangizo a Yehova ndi olungama,

9Kuopa Yehova ndiye chinthu changwiro,

10ndi a mtengowapatali kuposa golide,

11Mtumiki wanu amachenjezedwa nawo;

12Ndani angathe kudziwa zolakwa zake?

13Muteteze mtumiki wanunso ku machimo ochita akudziwa;

14Mawu a mʼkamwa mwanga ndi zolingalira za mu mtima mwanga

← Masalimo 18 Masalimo Masalimo 20 →