We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 149

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 148 Masalimo Masalimo 150 →

1Tamandani Yehova.

2Israeli asangalale mwa mlengi wake;

3Atamande dzina lake povina

4Pakuti Yehova amakondwera ndi anthu ake;

5Oyera mtima asangalale mu ulemu wake

6Matamando a Mulungu akhale pakamwa pawo,

7kubwezera chilango anthu a mitundu ina,

8kumanga mafumu awo ndi zingwe,

9kuchita zimene zinalembedwa zotsutsana nawo

← Masalimo 148 Masalimo Masalimo 150 →