1Tamandani Yehova.
2Israeli asangalale mwa mlengi wake;
3Atamande dzina lake povina
4Pakuti Yehova amakondwera ndi anthu ake;
5Oyera mtima asangalale mu ulemu wake
6Matamando a Mulungu akhale pakamwa pawo,
7kubwezera chilango anthu a mitundu ina,
8kumanga mafumu awo ndi zingwe,
9kuchita zimene zinalembedwa zotsutsana nawo