1Tamandani Yehova.
2Mutamandeni, inu angelo ake onse,
3Mutamandeni, inu dzuwa ndi mwezi,
4Mutamandeni, inu thambo la kumwambamwamba
5Zonse zitamande dzina la Yehova
6Iye anaziyika pa malo ake ku nthawi za nthawi;
7Tamandani Yehova pa dziko lapansi,
8inu zingʼaningʼani ndi matalala, chipale ndi mitambo,
9inu mapiri ndi zitunda zonse,
10inu nyama zakuthengo ndi ngʼombe zonse,
11Inu mafumu a dziko lapansi ndi anthu a mitundu yonse,
12Inu anyamata ndi anamwali,
13Onsewo atamande dzina la Yehova
14Iye wakwezera nyanga anthu ake,