We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 148

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 147 Masalimo Masalimo 149 →

1Tamandani Yehova.

2Mutamandeni, inu angelo ake onse,

3Mutamandeni, inu dzuwa ndi mwezi,

4Mutamandeni, inu thambo la kumwambamwamba

5Zonse zitamande dzina la Yehova

6Iye anaziyika pa malo ake ku nthawi za nthawi;

7Tamandani Yehova pa dziko lapansi,

8inu zingʼaningʼani ndi matalala, chipale ndi mitambo,

9inu mapiri ndi zitunda zonse,

10inu nyama zakuthengo ndi ngʼombe zonse,

11Inu mafumu a dziko lapansi ndi anthu a mitundu yonse,

12Inu anyamata ndi anamwali,

13Onsewo atamande dzina la Yehova

14Iye wakwezera nyanga anthu ake,

← Masalimo 147 Masalimo Masalimo 149 →