We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 147

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 146 Masalimo Masalimo 148 →

1Tamandani Yehova.

2Yehova akumanga Yerusalemu;

3Akutsogolera anthu osweka mtima

4Amadziwa chiwerengero cha nyenyezi,

5Yehova ndi wamkulu ndi wamphamvu kwambiri;

6Yehova amagwiriziza anthu odzichepetsa,

7Imbirani Yehova ndi mayamiko;

8Iye amaphimba mlengalenga ndi mitambo;

9Iye amapereka chakudya kwa ngʼombe

10Chikondwerero chake sichili mʼmphamvu za kavalo,

11Yehova amakondwera ndi amene amamuopa,

12Lemekeza Yehova, iwe Yerusalemu;

13pakuti Iye amalimbitsa mipiringidzo ya zipata zako

14Iye amabweretsa mtendere mʼmalire mwako

15Iyeyo amapereka lamulo pa dziko lapansi;

16Amagwetsa chisanu ngati ubweya

17Amagwetsa matalala ngati miyala.

18Amatumiza mawu ake ndipo chisanucho chimasungunuka;

19Iye anawulula mawu ake kwa Yakobo,

20Sanachitepo zimenezi kwa mtundu wina uliwonse wa anthu;

← Masalimo 146 Masalimo Masalimo 148 →