1Tamandani Yehova.
2Yehova akumanga Yerusalemu;
3Akutsogolera anthu osweka mtima
4Amadziwa chiwerengero cha nyenyezi,
5Yehova ndi wamkulu ndi wamphamvu kwambiri;
6Yehova amagwiriziza anthu odzichepetsa,
7Imbirani Yehova ndi mayamiko;
8Iye amaphimba mlengalenga ndi mitambo;
9Iye amapereka chakudya kwa ngʼombe
10Chikondwerero chake sichili mʼmphamvu za kavalo,
11Yehova amakondwera ndi amene amamuopa,
12Lemekeza Yehova, iwe Yerusalemu;
13pakuti Iye amalimbitsa mipiringidzo ya zipata zako
14Iye amabweretsa mtendere mʼmalire mwako
15Iyeyo amapereka lamulo pa dziko lapansi;
16Amagwetsa chisanu ngati ubweya
17Amagwetsa matalala ngati miyala.
18Amatumiza mawu ake ndipo chisanucho chimasungunuka;
19Iye anawulula mawu ake kwa Yakobo,
20Sanachitepo zimenezi kwa mtundu wina uliwonse wa anthu;