1Tamandani Yehova.
2Ndidzatamanda Yehova ndi moyo wanga wonse;
3Musamadalire mafumu,
4Pamene mizimu yawo yachoka, iwo amabwerera ku dothi;
5Wodala ndi amene thandizo lake ndi
6Wolenga kumwamba ndi dziko lapansi,
7Iye amachitira chilungamo anthu oponderezedwa
8Yehova amatsekula maso anthu osaona,
9Yehova amasamalira alendo
10Yehova ndiye Mfumu mpaka muyaya,