We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 146

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 145 Masalimo Masalimo 147 →

1Tamandani Yehova.

2Ndidzatamanda Yehova ndi moyo wanga wonse;

3Musamadalire mafumu,

4Pamene mizimu yawo yachoka, iwo amabwerera ku dothi;

5Wodala ndi amene thandizo lake ndi

6Wolenga kumwamba ndi dziko lapansi,

7Iye amachitira chilungamo anthu oponderezedwa

8Yehova amatsekula maso anthu osaona,

9Yehova amasamalira alendo

10Yehova ndiye Mfumu mpaka muyaya,

← Masalimo 145 Masalimo Masalimo 147 →