We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 145

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 144 Masalimo Masalimo 146 →

1Ndidzakukwezani Mulungu wanga, Mfumu yanga;

2Ndidzakutamandani tsiku ndi tsiku

3Yehova ndi wamkulu ndi woyenera matamando onse;

4Mʼbado wina udzayamikira ntchito yanu kwa mʼbado wina;

5Adzayankhula ulemerero wokongola waufumu wanu,

6Iwo adzafotokoza za mphamvu ya ntchito zanu zoopsa kwambiri,

7Adzakondwerera kuchuluka kwa ubwino wanu,

8Yehova ndi wokoma mtima ndi wachifundo,

9Yehova ndi wabwino kwa onse;

10Zonse zimene munazipanga zidzakutamandani, Inu Yehova;

11Iwo adzafotokoza za ulemerero wa ufumu wanu

12kuti anthu onse adziwe za machitidwe anu amphamvu

13Ufumu wanu ndi ufumu wamuyaya,

14Yehova amagwiriziza onse amene akugwa

15Maso a onse amayangʼana kwa Inu,

16Mumatsekula dzanja lanu

17Yehova ndi wolungama mʼnjira zake zonse,

18Yehova ali pafupi ndi onse amene amamuyitana,

19Iye amakwaniritsa zokhumba za iwo amene amamuopa;

20Yehova amayangʼana onse amene amamukonda

21Pakamwa panga padzayankhula zotamanda Yehova.

← Masalimo 144 Masalimo Masalimo 146 →