1Ndidzakukwezani Mulungu wanga, Mfumu yanga;
2Ndidzakutamandani tsiku ndi tsiku
3Yehova ndi wamkulu ndi woyenera matamando onse;
4Mʼbado wina udzayamikira ntchito yanu kwa mʼbado wina;
5Adzayankhula ulemerero wokongola waufumu wanu,
6Iwo adzafotokoza za mphamvu ya ntchito zanu zoopsa kwambiri,
7Adzakondwerera kuchuluka kwa ubwino wanu,
8Yehova ndi wokoma mtima ndi wachifundo,
9Yehova ndi wabwino kwa onse;
10Zonse zimene munazipanga zidzakutamandani, Inu Yehova;
11Iwo adzafotokoza za ulemerero wa ufumu wanu
12kuti anthu onse adziwe za machitidwe anu amphamvu
13Ufumu wanu ndi ufumu wamuyaya,
14Yehova amagwiriziza onse amene akugwa
15Maso a onse amayangʼana kwa Inu,
16Mumatsekula dzanja lanu
17Yehova ndi wolungama mʼnjira zake zonse,
18Yehova ali pafupi ndi onse amene amamuyitana,
19Iye amakwaniritsa zokhumba za iwo amene amamuopa;
20Yehova amayangʼana onse amene amamukonda
21Pakamwa panga padzayankhula zotamanda Yehova.