1Atamandike Yehova Thanthwe langa,
2Iye ndiye Mulungu wanga wachikondi ndi malo anga otetezedwa,
3Inu Yehova, munthu nʼchiyani kuti mumamusamalira,
4Munthu ali ngati mpweya;
5Ngʼambani mayiko akumwamba, Inu Yehova, ndipo tsikani pansi;
6Tumizani zingʼaningʼani ndi kubalalitsa adani;
7Tambasulani dzanja lanu kuchokera kumwamba;
8amene pakamwa pawo ndi podzala ndi mabodza,
9Ndidzakuyimbirani nyimbo yatsopano Inu Mulungu;
10kwa Iye amene amapambanitsa mafumu,
11Landitseni ndi kundipulumutsa,
12Ndipo ana aamuna pa chinyamata chawo
13Nkhokwe zathu zidzakhala zodzaza
14Ngʼombe zathu zidzanyamula katundu wolemera.
15Odala anthu amene adzalandira madalitso awa;