We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 144

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 143 Masalimo Masalimo 145 →

1Atamandike Yehova Thanthwe langa,

2Iye ndiye Mulungu wanga wachikondi ndi malo anga otetezedwa,

3Inu Yehova, munthu nʼchiyani kuti mumamusamalira,

4Munthu ali ngati mpweya;

5Ngʼambani mayiko akumwamba, Inu Yehova, ndipo tsikani pansi;

6Tumizani zingʼaningʼani ndi kubalalitsa adani;

7Tambasulani dzanja lanu kuchokera kumwamba;

8amene pakamwa pawo ndi podzala ndi mabodza,

9Ndidzakuyimbirani nyimbo yatsopano Inu Mulungu;

10kwa Iye amene amapambanitsa mafumu,

11Landitseni ndi kundipulumutsa,

12Ndipo ana aamuna pa chinyamata chawo

13Nkhokwe zathu zidzakhala zodzaza

14Ngʼombe zathu zidzanyamula katundu wolemera.

15Odala anthu amene adzalandira madalitso awa;

← Masalimo 143 Masalimo Masalimo 145 →