1Yehova imvani pemphero langa,
2Musazenge mlandu mtumiki wanu,
3Mdani akundithamangitsa,
4Choncho mzimu wanga ukufowoka mʼkati mwanga;
5Ndimakumbukira masiku amakedzana;
6Ndatambalitsa manja anga kwa Inu;
7Yehova ndiyankheni msanga;
8Lolani kuti mmawa ubweretse mawu achikondi chanu chosasinthika,
9Pulumutseni kwa adani anga, Inu Yehova,
10Phunzitseni kuchita chifuniro chanu,
11Sungani moyo wanga Inu Yehova chifukwa cha dzina lanu;
12Mwa chikondi chanu chosasinthika khalitsani chete adani anga;