We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 143

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 142 Masalimo Masalimo 144 →

1Yehova imvani pemphero langa,

2Musazenge mlandu mtumiki wanu,

3Mdani akundithamangitsa,

4Choncho mzimu wanga ukufowoka mʼkati mwanga;

5Ndimakumbukira masiku amakedzana;

6Ndatambalitsa manja anga kwa Inu;

7Yehova ndiyankheni msanga;

8Lolani kuti mmawa ubweretse mawu achikondi chanu chosasinthika,

9Pulumutseni kwa adani anga, Inu Yehova,

10Phunzitseni kuchita chifuniro chanu,

11Sungani moyo wanga Inu Yehova chifukwa cha dzina lanu;

12Mwa chikondi chanu chosasinthika khalitsani chete adani anga;

← Masalimo 142 Masalimo Masalimo 144 →