1Tamandani Yehova.
2Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu;
3Mutamandeni poyimba malipenga,
4Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina,
5Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga,
6Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova.
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja
1Tamandani Yehova.
2Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu;
3Mutamandeni poyimba malipenga,
4Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina,
5Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga,
6Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova.