We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 140

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 139 Masalimo Masalimo 141 →

1Landitseni Yehova kwa anthu oyipa;

2amene mu mtima mwawo amakonza zinthu zoyipa

3Iwo amanola malilime awo kukhala akuthwa ngati a njoka;

4Tetezeni Inu Yehova, kwa anthu oyipa;

5Anthu odzikuza anditchera msampha mobisika;

6Inu Yehova, ine ndikuti, “Ndinu Mulungu wanga.”

7Inu Ambuye Wamphamvuzonse, Mpulumutsi wanga wamphamvu,

8Musawapatse anthu oyipa zokhumba zawo, Inu Yehova;

9Mitu ya amene andizungulira

10Makala amoto agwere pa iwo;

11Musalole kuti anthu achipongwe akhazikike mʼdziko;

12Ndikudziwa kuti Yehova amapereka chiweruzo cholungama kwa anthu osauka,

13Zoonadi anthu olungama adzatamanda dzina lanu,

← Masalimo 139 Masalimo Masalimo 141 →