1Inu Yehova ndikukuyitanani; bwerani msanga kwa ine.
2Pemphero langa lifike kwa Inu ngati lubani;
3Yehova ikani mlonda pakamwa panga;
4Musalole kuti mtima wanga ukokedwere ku zoyipa;
5Munthu wolungama andikanthe, chimenecho ndiye chifundo;
6Olamulira awo adzaponyedwa pansi kuchokera pa malo okwera kwambiri,
7Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza,
8Koma maso anga akupenyetsetsa Inu Ambuye Wamphamvuzonse;
9Mundipulumutse ku misampha imene anditchera,
10Anthu oyipa akodwe mʼmaukonde awo,