We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 141

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 140 Masalimo Masalimo 142 →

1Inu Yehova ndikukuyitanani; bwerani msanga kwa ine.

2Pemphero langa lifike kwa Inu ngati lubani;

3Yehova ikani mlonda pakamwa panga;

4Musalole kuti mtima wanga ukokedwere ku zoyipa;

5Munthu wolungama andikanthe, chimenecho ndiye chifundo;

6Olamulira awo adzaponyedwa pansi kuchokera pa malo okwera kwambiri,

7Iwo adzati, “Monga momwe nkhuni zimamwazikira akaziwaza,

8Koma maso anga akupenyetsetsa Inu Ambuye Wamphamvuzonse;

9Mundipulumutse ku misampha imene anditchera,

10Anthu oyipa akodwe mʼmaukonde awo,

← Masalimo 140 Masalimo Masalimo 142 →