1Chitsiru chimati mu mtima mwake,
2Yehova kumwamba wayangʼana pansi,
3Onse atembenukira kumbali,
4Kodi anthu ochita zoyipawa sadziwa chilichonse?
5Awo ali apowo, agwidwa ndi mantha aakulu,
6Inu ochita zoyipa mumalepheretsa chikonzero cha anthu osauka,
7Ndithu, chipulumutso cha Israeli chidzachokera ku Ziyoni!