1Yehova, ndani angathe kukhala mʼmalo anu opatulika?
2Munthu wa makhalidwe abwino,
3ndipo mʼkamwa mwake simutuluka mawu osinjirira,
4amene sapereka ulemu kwa munthu woyipa.
5amene amakongoletsa ndalama zake popanda chiwongoladzanja
Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja
1Yehova, ndani angathe kukhala mʼmalo anu opatulika?
2Munthu wa makhalidwe abwino,
3ndipo mʼkamwa mwake simutuluka mawu osinjirira,
4amene sapereka ulemu kwa munthu woyipa.
5amene amakongoletsa ndalama zake popanda chiwongoladzanja