We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 13

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 12 Masalimo Masalimo 14 →

1Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale?

2Ndidzalimbana ndi maganizo anga

3Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga.

4mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,”

5Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika;

6Ine ndidzayimbira Yehova

← Masalimo 12 Masalimo Masalimo 14 →