1Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale?
2Ndidzalimbana ndi maganizo anga
3Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga.
4mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,”
5Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika;
6Ine ndidzayimbira Yehova