1Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika;
2Aliyense amanamiza mʼbale wake;
3Inu Yehova tsekani milomo yonse yachinyengo
4Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu;
5“Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvu
6Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro
7Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo
8Oyipa amangoyendayenda ponseponse