1Ndidzakuyamikani Yehova ndi mtima wanga wonse;
2Ndidzagwada kuyangʼana ku Nyumba yanu yoyera
3Pamene ndinayitana, munandiyankha;
4Mafumu onse a dziko lapansi akuyamikeni Yehova,
5Iwo ayimbe za njira za Yehova,
6Ngakhale kuti Yehova ngokwezeka, amasamalira odzichepetsa,
7Ngakhale ndiyende pakati pa masautso,
8Yehova adzakwaniritsa cholinga chake pa ine;