We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 138

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 137 Masalimo Masalimo 139 →

1Ndidzakuyamikani Yehova ndi mtima wanga wonse;

2Ndidzagwada kuyangʼana ku Nyumba yanu yoyera

3Pamene ndinayitana, munandiyankha;

4Mafumu onse a dziko lapansi akuyamikeni Yehova,

5Iwo ayimbe za njira za Yehova,

6Ngakhale kuti Yehova ngokwezeka, amasamalira odzichepetsa,

7Ngakhale ndiyende pakati pa masautso,

8Yehova adzakwaniritsa cholinga chake pa ine;

← Masalimo 137 Masalimo Masalimo 139 →