1Mʼmbali mwa mitsinje ya ku Babuloni tinakhala pansi ndi kulira
2Kumeneko, pa mitengo ya misondozi
3pakuti anthu otigwira ukapolo anatipempha kuti tiyimbe nyimbo.
4Tingayimbe bwanji nyimbo za Yehova
5Ndikakuyiwala iwe Yerusalemu,
6Lilime langa limamatire ku nkhama za mʼkamwa mwanga
7Kumbukirani, Inu Yehova, zimene Aedomu anachita
8Iwe mwana wa mkazi wa Babuloni, woyenera kuwonongedwa,
9Amene adzagwira makanda ako