We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Masalimo 137

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Masalimo 136 Masalimo Masalimo 138 →

1Mʼmbali mwa mitsinje ya ku Babuloni tinakhala pansi ndi kulira

2Kumeneko, pa mitengo ya misondozi

3pakuti anthu otigwira ukapolo anatipempha kuti tiyimbe nyimbo.

4Tingayimbe bwanji nyimbo za Yehova

5Ndikakuyiwala iwe Yerusalemu,

6Lilime langa limamatire ku nkhama za mʼkamwa mwanga

7Kumbukirani, Inu Yehova, zimene Aedomu anachita

8Iwe mwana wa mkazi wa Babuloni, woyenera kuwonongedwa,

9Amene adzagwira makanda ako

← Masalimo 136 Masalimo Masalimo 138 →