1Ndikweza maso anga ku mapiri;
2Thandizo langa limachokera kwa Yehova,
3Sadzalola kuti phazi lako literereke;
4Taonani, Iye amene amasunga Israeli
5Yehova ndiye amene amakusunga;
6Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana,
7Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse;
8Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako;