1Ndinakondwera atandiwuza kuti,
2Mapazi athu akuyima mʼzipata
3Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda
4Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko,
5Kumeneko anayikako mipando yaufumu yachiweruzo,
6Pemphererani mtendere wa Yerusalemu:
7Mukhale mtendere mʼkati mwa makoma ako,
8Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga
9Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu,