1Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga,
2Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza,
3Kodi adzakuchitani chiyani,
4Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo,
5Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki,
6Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati
7Ine ndine munthu wamtendere;